2 Samueli 12:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsono Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Atafika kwa Davide anati, “Panali anthu awiri mʼmizinda ina, wina wolemera ndi wina wosauka. Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Ndipo Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Ndipo anafika kwa iye nanena naye, Mu mzinda wina munali anthu awiri; wina wolemera, wina wosauka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Ndipo anafika kwa iye nanena naye, Pa mudzi wina panali anthu awiri; wina wolemera, wina wosauka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pambuyo pake Chauta adatuma mneneri Natani kwa Davide. Natani atafika kwa Davide, adamphera fanizo lakuti, “Mu mzinda wina munali anthu aŵiri, wina wolemera, wina wosauka. Onani mutuwo |