2 Samueli 1:22 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “Pa magazi a ophedwa, pa mnofu wa amphamvu, uta wa Yonatani sunabwerere, lupanga la Sauli silinabwere chabe. Onani mutuwoBuku Lopatulika22 Uta wa Yonatani sunabwerere, ndipo lupanga la Saulo silinabwerere chabe, pa mwazi wa ophedwa, pa mafuta a amphamvuwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Uta wa Yonatani sunabwerera, ndipo lupanga la Saulo silinabwerera chabe, pa mwazi wa ophedwa, pa mafuta a amphamvuwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 “Uta wa Yonatani sudabwereko chabe osakhetsa magazi a anthu osabayako ankhondo amphamvu. Ndipo lupanga la Saulo silidabwereko chabe osapha anthu. Onani mutuwo |