Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Samueli 3:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Yehova anayitana Samueli. Iye anayankha kuti, “Wawa.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Pamenepo Yehova anaitana Samuele; ndipo iye anayankha kuti, Ndili pano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Pamenepo Yehova anaitana Samuele; ndipo iye anayankha kuti, Ndili pano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono Chauta adaitana kuti, “Samuele, Samuele!” Iye adayankha kuti, “Ŵaŵa!”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 3:4
10 Mawu Ofanana  

Nthawi ina zitatha izi, Mulungu anamuyesa Abrahamu. Iye anati, “Abrahamu!” Ndipo iye anayankha kuti, “Ee Ambuye.”


Koma mngelo wa Yehova anayitana Abrahamu kuchokera kumwamba nati, “Abrahamu! Abrahamu!” Iye anayankha kuti, “Ee Ambuye.”


Mose ndi Aaroni anali ena mwa ansembe ake, Samueli anali pamodzi ndi iwo amene anayitana pa dzina lake; iwo anayitana Yehova ndipo Iyeyo anawayankha.


Yehova ataona kuti Mose anapatuka kuti adzaonetsetse, Mulungu anamuyitana Mose kuchokera mʼchitsambamo nati, “Mose! Mose!” Ndipo anayankha, “Wawa.”


Kenaka ndinamva mawu a Ambuye akuti, “Kodi ndidzatuma yani? Ndipo ndani adzapite mʼmalo mwathu?” Ndipo ine ndinati, “Ndilipo. Tumeni!”


Iye anagwa pansi ndipo anamva mawu akuti, “Saulo, Saulo ukundizunziranji Ine?”


Ndipo Mulungu mu mpingo anayika poyamba atumwi, kachiwiri aneneri, kachitatu aphunzitsi, kenaka ochita zozizwitsa, ena a mphatso zamachiritso, ena a mphatso yothandiza anzawo, ena a mphatso yotsogolera ndiponso ena a mphatso ya malilime.


Ndipo iyeyo anathamangira kwa Eli ndipo anati, “Ndabwera ndamva kuyitana.” Koma Eli anati, “Ine sindinakuyitane, bwerera kagone.” Ndipo iye anapita kukagona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa