Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Samueli 10:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Adzakupatsa moni ndi kukupatsa malofu awiri a buledi. Iwe udzalandire bulediyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Iwowa adzakupatsani moni, ndi kukupatsani mikate iwiri; imeneyi mudzailandira m'manja mwao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Iwowa adzakupatsani moni, ndi kukupatsani mikate iwiri; imeneyi mudzailandira m'manja mwao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Atakupatsa moni, akuninkhako mitanda iŵiri ya buledi, iwe uilandire.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 10:4
4 Mawu Ofanana  

Choncho anthuwa anapatuka napita ku nyumba ya Mika kumene mnyamata, Mlevi uja ankakhala ndipo anamufunsa za mmene zinthu zilili.


“Ndipo udzapyola pamenepo ndi kufika ku mtengo wa thundu wa ku Tabori. Kumeneko udzakumana ndi anthu atatu akupita kukapereka nsembe ku Nyumba ya Mulungu ku Beteli. Mmodzi adzakhala atanyamula ana ambuzi atatu, wina atanyamula malofu atatu a buledi, ndi winayo atanyamula thumba la vinyo.


“Pambuyo pake, udzafike ku Gibeyati-Elohimu, kumene kuli gulu la ankhondo la Afilisti. Pamene ukuyandikira mzindawo, udzakumana ndi gulu la aneneri akutsika kuchokera ku phiri, akuyimba zeze, ngʼoma, zitoliro ndi pangwe, ndiponso akulosera.


Choncho Yese anatenga bulu namunyamulitsa buledi, thumba la vinyo ndi mwana wambuzi mmodzi. Zonsezi anamupatsa mwana wake Davide kuti akapereke kwa Sauli.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa