Zekariya 9:15 - Buku Lopatulika15 Yehova wa makamu adzawatchinjiriza; ndipo adzadza, nadzapondereza miyala yoponyera; ndipo adzamva, nadzachita phokoso ngati avinyo; ndipo adzadzazidwa ngati mbale, ngati ngodya za guwa la nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Yehova wa makamu adzawatchinjiriza; ndipo adzadza, nadzapondereza miyala yoponyera; ndipo adzamva, nadzachita phokoso ngati avinyo; ndipo adzadzazidwa ngati mbale, ngati ngodya za guwa la nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Chauta Wamphamvuzonse adzakhala chishango chao. Iwowo adzapambana ndi kugonjetsa adani ao poponya miyala chabe. Adzamwa magazi ao nkumafuula ngati okhuta vinyo. Magaziwo adzachita kuyenderera ngati magazi a nsembe, othira ndi mkhate pa guwa popembedza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 ndipo Yehova Wamphamvuzonse adzawateteza. Iwo adzawononga ndipo adzagonjetsa ndi miyala ya legeni. Adzamwa magazi ndi kubangula ngati amwa vinyo; magazi adzayenderera ngati a mʼmbale yowazira magazi pa ngodya za guwa lansembe. Onani mutuwo |