Zekariya 9:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Yehova adzaoneka pamwamba pao, ndi muvi wake udzatuluka ngati mphezi; ndipo Ambuye Mulungu adzaomba lipenga, nadzayenda ndi akamvulumvulu a kumwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Yehova adzaoneka pamwamba pao, ndi muvi wake udzatuluka ngati mphezi; ndipo Ambuye Mulungu adzaomba lipenga, nadzayenda ndi akavumbulu a kumwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono Chauta adzaonekera anthu ake, ndipo mivi yake adzaiponya ngati zing'aning'ani. Ambuye Chauta adzaliza lipenga, ndipo adzayenda m'kamvulumvulu wochokera kumwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pamenepo Yehova adzaonekera kwa anthu ake; mivi yake idzangʼanima ngati chingʼaningʼani. Ambuye Yehova adzaliza lipenga; ndipo adzayenda mu mkuntho wochokera kummwera, Onani mutuwo |