Zekariya 9:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti ndadzikokera Yuda, ndadzaza uta ndi Efuremu; ndipo ndidzautsa ana ako, Ziyoni, alimbane nao ana ako, Yavani, ndipo ndidzakuyesa lupanga la ngwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti ndadzikokera Yuda, ndadzaza uta ndi Efuremu; ndipo ndidzautsa ana ako, Ziyoni, alimbane nao ana ako, Yavani, ndipo ndidzakuyesa lupanga la ngwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Ndidzakoka Yuda ngati uta wanga, Efuremu adzakhala ngati muvi wake. Ndidzatenga ana ako, iwe Ziyoni, kuti alimbane ndi ana ako, iwe Grisi; ndidzakugwira ngati lupanga la wankhondo wamphamvu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndidzakoka Yuda monga ndimakokera uta wanga, ndipo Efereimu ndiye muvi wake. Ndidzadzutsa ana ako iwe Ziyoni, kulimbana ndi ana ako iwe Grisi, ndipo ndidzakusandutsa iwe lupanga la munthu wankhondo. Onani mutuwo |