Zekariya 9:11 - Buku Lopatulika11 Iwenso, chifukwa cha mwazi wa pangano lako ndinatulutsa andende ako m'dzenje m'mene mulibe madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Iwenso, chifukwa cha mwazi wa pangano lako ndinatulutsa andende ako m'dzenje m'mene mulibe madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta akuti, “Tsono kunena za inu, chifukwa cha chipangano changa ndi inu, chimene nsembe zamagazi zidachitsimikiza, ndidzaŵatulutsa m'dzenje lopanda madzi anthu anu amene ali ngati akapolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Tsono kunena za iwe, chifukwa cha magazi a pangano lako ndi Ine, ndidzamasula amʼndende ako, ndidzawatulutsa mʼdzenje lopanda madzi. Onani mutuwo |