Zekariya 8:23 - Buku Lopatulika23 Atero Yehova wa makamu: Kudzachitika masiku awo amuna khumi adzagwira, ndiwo a manenedwe onse a amitundu, inde adzagwira mkawo wa munthu ali Myuda, ndi kuti, Tidzamuka nanu, pakuti tamva kuti Mulungu ali ndi inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Atero Yehova wa makamu: Kudzachitika masiku awo amuna khumi adzagwira, ndiwo a manenedwe onse a amitundu, inde adzagwira mkawo wa munthu ali Myuda, ndi kuti, Tidzamuka nanu, pakuti tamva kuti Mulungu ali ndi inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 “Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikunena kuti, pa masiku amenewo anthu khumi ochokera ku mitundu ya anthu a zilankhulo zosiyana adzagwira mkanjo wa Myuda ndi kunena kuti, ‘Tipite nao, chifukwa tamva kuti Mulungu ali nanu.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Masiku amenewo anthu khumi ochokera ku mitundu ya anthu a ziyankhulo zosiyana adzagwira mkanjo wa Myuda ndi kunena kuti, ‘Tipite nawo, chifukwa tamva kuti Mulungu ali nanu.’ ” Onani mutuwo |