Zekariya 8:21 - Buku Lopatulika21 ndi okhala m'mzinda umodzi adzamuka kumzinda wina, ndi kuti, Tiyeni msanga kukapepeza Yehova, ndi kufunafuna Yehova wa makamu; ndimuka inenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ndi okhala m'mudzi umodzi adzamuka kumudzi wina, ndi kuti, Tiyeni msanga kukapepeza Yehova, ndi kufunafuna Yehova wa makamu; ndimuka inenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Anthu a mzinda wina adzapita ku mzinda wina, kukanena kuti, ‘Tiyeni mwamsanga tikapemphe chifundo kwa Chauta, tikapembedze Chauta Wamphamvuzonse. Ifeyo tikupita komweko.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 ndipo nzika za mzinda wina zidzapita ku mzinda wina, kukanena kuti, ‘Tiyeni mwamsanga tikapemphe madalitso kwa Yehova ndi kukapembedza Yehova Wamphamvuzonse. Inenso ndikupita kumeneko.’ Onani mutuwo |