Zekariya 8:20 - Buku Lopatulika20 Atero Yehova wa makamu: Kudzachitikanso kuti mitundu ya anthu, ndi okhalamo m'mizinda yambiri adzafika, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Atero Yehova wa makamu: Kudzachitikanso kuti mitundu ya anthu, ndi okhalamo m'midzi yambiri adzafika, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Zimene ndikunena Ine Chauta Wamphamvuzonse ndi izi: Anthu a mitundu yambiri ndi anthu okhala m'mizinda yambiri adzabweradi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu a mitundu yambiri ndi anthu okhala mʼmizinda yambiri adzabwerabe, Onani mutuwo |