Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Zekariya 8:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Chauta Wamphamvuzonse adandipatsa uthenga uwu wakuti, “Ine Chauta Wamphamvuzonse mau anga ndi aŵa:

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Yehova Wamphamvuzonse anayankhulanso nane.

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 8:18
5 Mawu Ofanana  

ndipo musalingirira choipa m'mtima mwanu yense pa mnzake; nimusakonde lumbiro lonama; pakuti izi zonse ndidana nazo, ati Yehova.


Atero Yehova wa makamu: Kusala kwa mwezi wachinai, ndi kusala kwa mwezi wachisanu, ndi kusala kwa mwezi wachisanu ndi chiwiri, ndi kusala kwa mwezi wakhumi kukhale kwa nyumba ya Yuda chimwemwe ndi chikondwerero, ndi nyengo zoikika zosekerera; chifukwa chake kondani choonadi ndi mtendere.


Atero Yehova wa makamu: Alimbike manja anu, inu akumva masiku ano mau awa pakamwa pa aneneri amene anakhalako tsiku lakuikidwa maziko a nyumba ya Yehova wa makamu, ndiyo Kachisi, kuti amangidwe.


Koma anali mu Yerusalemu okhalako Ayuda, amuna opembedza, ochokera kumtundu uliwonse pansi pa thambo.


ndi kusanthula nthawi yiti, kapena nthawi yanji Mzimu wa Khristu wokhala mwa iwo analozera, pakuchitiratu umboni wa masautso a Khristu, ndi ulemerero wotsatana nao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa