Zekariya 8:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti atero Yehova wa makamu: Monga ndinalingirira kuchitira inu choipa, muja makolo anu anautsa mkwiyo wanga, ati Yehova wa makamu, ndipo sindinawaleke; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti atero Yehova wa makamu: Monga ndinalingirira kuchitira inu choipa, muja makolo anu anautsa mkwiyo wanga, ati Yehova wa makamu, ndipo sindinawaleka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Ine Chauta Wamphamvuzonse mau anga ndi aŵa: Paja ndidaatsimikiza mtima kuti ndikuwonongeni, chifukwa chakuti makolo anu adaandikwiyitsa, ndipo sindidafune kukhululuka. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Monga ndinatsimikiza mtima kubweretsa choyipa pa inu, komanso osakuchitirani chisoni pamene makolo anu anandikwiyitsa,” akutero Yehova, Onani mutuwo |