Zekariya 6:11 - Buku Lopatulika11 ndipo utenge siliva ndi golide, nupange akorona, nuwaike pamutu pa Yoswa mwana wa Yehozadaki mkulu wa ansembe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 ndipo utenge siliva ndi golide, nupange akorona, nuwaike pamutu pa Yoswa mwana wa Yehozadaki mkulu wa ansembe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Siliva ndi golide amene ulandireyo upangire chisoti chaufumu. Chisoticho uchiike pamutu pa mkulu wa ansembe uja Yoswa, mwana wa Yehozadaki. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Tenga siliva ndi golide upange chipewa chaufumu, ndipo uchiyike pamutu pa mkulu wa ansembe, Yoswa mwana wa Yehozadaki. Onani mutuwo |