Zekariya 14:7 - Buku Lopatulika7 koma lidzakhala tsiku la pa lokha lodziwika ndi Yehova; palibe usana, palibe usiku; koma kudzatero kuti madzulo kudzati mbee. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 koma lidzakhala tsiku la pa lokha lodziwika ndi Yehova; palibe usana, palibe usiku; koma kudzatero kuti madzulo kudzati mbee. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Lidzakhala tsiku la kuŵala kokhakokha, osakhala usana, osakhala usiku, chifukwa ndi madzulo omwe kuzidzaŵalabe. Tsiku limene zidzachitike zimenezi ndi Chauta yekha akulidziŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Lidzakhala tsiku lapaderadera, silidzakhala usana kapena usiku; tsiku limeneli akulidziwa ndi Yehova yekha. Ikadzafika nthawi ya madzulo, kudzakhala kukuwalabe. Onani mutuwo |