Zekariya 14:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anthu adzakhala m'menemo, ndipo sipadzakhalanso kuonongetsa; koma Yerusalemu adzakhala mosatekeseka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anthu adzakhala m'menemo, ndipo sipadzakhalanso kuonongetsa; koma Yerusalemu adzakhala mosatekeseka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Anthu adzakhala ku Yerusalemu mwamtendere, poti sadzaopsezedwanso ndi chiwonongeko kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mʼmenemo mudzakhala anthu; sadzawonongedwanso. Yerusalemu adzakhala pa mtendere. Onani mutuwo |