Zekariya 14:1 - Buku Lopatulika1 Taonani likudza tsiku la Yehova, limene zofunkha zako zidzagawanika pakati pako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Taonani likudza tsiku la Yehova, limene zofunkha zako zidzagawanika pakati pako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Onani, tsiku likubwera, la Chauta, pamene zinthu zomwe adani ako adakulanda, azidzagaŵana iwe uli pomwepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Taonani tsiku la Yehova likubwera pamene zinthu zimene adani ako anakulanda azidzagawana iwe ukuona. Onani mutuwo |