Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Zekariya 11:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo Yehova anati kwa ine, Dzitengerenso zipangizo za mbusa wopusa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo Yehova anati kwa ine, Dzitengerenso zipangizo za mbusa wopusa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tsono Chauta adandiwuza kuti, “Tenganso zida za mbusa, mbusa wake wopandapake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Pamenepo Yehova anayankhula nane kuti, “Tenganso zida za mʼbusa wopusa.

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 11:15
10 Mawu Ofanana  

Tsoka abusa amene athetsa nabalalitsa nkhosa za busa langa! Ati Yehova.


Aneneri ako anakuonera masomphenya achabe ndi opusa; osawulula mphulupulu yako kuti abweze undende wako, koma anakuonera manenero achabe ndi opambutsa.


Atero Ambuye Yehova, Tsoka aneneri opusawo akutsata mzimu waowao, chinkana sanaone kanthu.


Ndipo mau a Yehova anandidzera, akuti,


Tsoka mbusa wopanda pake, wakusiya zoweta! Lupanga padzanja lake, ndi pa diso lake la kumanja; dzanja lake lidzauma konse, ndi diso lake lamanja lidzada bii.


Kawalekeni iwo, ali atsogoleri akhungu. Ndipo ngati wakhungu amtsogolera wakhungu, onse awiri adzagwa m'mbuna.


Inu opusa, ndi akhungu: pakuti choposa nchiti, golide kodi, kapena Kachisi amene ayeretsa golideyo?


Opusa inu, kodi Iye wopanga kunja kwake sanapangenso m'kati mwake?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa