Zekariya 11:14 - Buku Lopatulika14 Pamenepo ndinadula ndodo yanga ina, ndiyo Chomanganitsa, kuti ndithetse chibale cha pakati pa Yuda ndi Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pamenepo ndinadula ndodo yanga ina, ndiyo Chomanganitsa, kuti ndithetse chibale cha pakati pa Yuda ndi Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kenaka ndidathyolanso ndodo ina ija yotchedwa “Umodzi,” kusonyeza kuthetsa ubale pakati pa Yuda ndi Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kenaka ndinathyola ndodo yanga yachiwiri yotchedwa Umodzi, kuthetsa ubale pakati pa Yuda ndi Israeli. Onani mutuwo |