Zekariya 11:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo linathyoka tsikulo, momwemo zonyankhalala za zoweta, zakundisamalira Ine, zinadziwa kuti ndiwo mau a Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo linathyoka tsikulo, momwemo zonyankhalala za zoweta, zakundisamalira Ine, zinadziwa kuti ndiwo mau a Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Motero chipanganocho chidatha tsiku limenelo, ndipo ochita malonda a nkhosa aja, amene ankangondiyang'anitsitsa, adazindikira kuti zonse zimene ndinkachita zinali zochokera kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Linaphwanyidwa tsiku limenelo ndipo nkhosa zosautsidwa zimene zimandiyangʼanitsitsa zinadziwa kuti anali mawu a Yehova. Onani mutuwo |