Zefaniya 3:15 - Buku Lopatulika15 Yehova wachotsa maweruzo ako, anataya kunja mdani wako; mfumu ya Israele, Yehova, ali pakati pako, sudzaopanso choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Yehova wachotsa maweruzo ako, anataya kunja mdani wako; mfumu ya Israele, Yehova, ali pakati pako, sudzaopanso choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Chauta wachotsa chilango chanu. Wapirikitsa adani anu. Chauta, Mfumu ya Israele, ali nanu pamodzi. Simudzaopanso choipa chilichonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Yehova wachotsa chilango chako, wabweza mdani wako. Yehova, Mfumu ya Israeli, ali pakati pako; sudzaopanso chilichonse. Onani mutuwo |