Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 9:8 - Buku Lopatulika

8 Koma anati kwa Yoswa, Ndife akapolo anu. Pamenepo Yoswa anati kwa iwo, Ndinu ayani? Ndipo mufuma kuti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Koma anati kwa Yoswa, Ndife akapolo anu. Pamenepo Yoswa anati kwa iwo, Ndinu ayani? Ndipo mufuma kuti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Iwo adauza Yoswa kuti, “Ife ndife akapolo anu.” Tsono Yoswa adaŵafunsa kuti, “Kodi inu ndinu yani? Mwachoka kuti?” Anthuwo adamuuza nkhani yonse, adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Iwo anati kwa Yoswa, “Ife ndife akapolo anu.” Tsono Yoswa anawafunsa kuti, “Inu ndinu yani ndipo mukuchokera kuti?”

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 9:8
9 Mawu Ofanana  

Ndipo iye wakuyang'anira nyumba, ndi iye wakuyang'anira mzinda, ndi akuluakulu, ndi iwo akulera anawo, anatumiza kwa Yehu, ndi kuti, Ife ndife akapolo anu ndi zonse mutiuza tidzachita; sitidzalonga munthu yense mfumu; chokomera pamaso panu chitani.


Ndipo kudzali, ukakubwezerani mau a mtendere, ndi kukutsegulirani, pamenepo anthu onse opezeka m'mwemo akhale akapolo anu, nadzakugwirirani ntchito yathangata.


Ndipo amuna a ku Gibiyoni anatumira Yoswa mau kuchigono ku Giligala, ndi kuti, Musalekerere akapolo anu; mutikwerere msanga, ndi kutipulumutsa, ndi kutithandiza; pakuti mafumu onse a Aamori, akukhala kumapiri atisonkhanira.


Ndipo akulu athu ndi nzika zonse za m'dziko mwathu zidanena nafe ndi kuti, Mutenge m'dzanja lanu kamba wa paulendo, kakomane naoni, nimunene nao, Ndife akapolo anu; ndipo tsopano mupangane nafe.


Ndipo tsopano mukhale otembereredwa, palibe mmodzi wa inu adzamasuka wosakhala kapolo, ndi kutemera nkhuni, ndi kutungira madzi nyumba ya Mulungu wanga.


Ndipo tsopano, taonani, tili m'dzanja lanu; monga muyesa chokoma ndi choyenera kutichitira ife, chitani.


Ndipo tsiku lija Yoswa anawasandutsa akutema nkhuni, ndi otungira madzi msonkhanowo, ndi guwa la nsembe la Yehova, mpaka lero lino, pamalopo akadzasankha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa