Yoswa 9:5 - Buku Lopatulika5 ndi nsapato zakale za zigamba pa mapazi ao, ndipo zinavala nsanza; ndi mikate yonse ya kamba wao inali youma ndi yoyanga nkhungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndi nsapato zakale za zigamba pa mapazi ao, nizivala nsanza; ndi mikate yonse ya kamba wao inali youma ndi yoyanga nkhungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adavala nsapato zothaitha za zigamba zokhazokha, ndiponso zovala zansanza. Buledi amene adatenga anali wouma ndi wachuku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Anthuwa anavala nsapato zakutha ndi zazigamba ndiponso anavala sanza. Buledi wawo yense anali wowuma ndi wowola. Onani mutuwo |