Yoswa 8:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yoswa anawatuma, namuka iwo kulowa m'molalira, nakhala pakati pa Betele ndi Ai, kumadzulo kwa Ai; koma Yoswa anakhala mwa anthu usiku uja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yoswa anawatuma, namuka iwo kulowa m'molalira, nakhala pakati pa Betele ndi Ai, kumadzulo kwa Ai; koma Yoswa anakhala mwa anthu usiku uja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Motero Yoswa adaŵatuma, ndipo iwo adapita ku malo obisalakowo kukaulalira mzindawo. Malowo anali cha kuzambwe kwa Ai, pakati pa Ai ndi Betele. Koma Yoswa ndi gulu lake lankhondo adakhala m'zithando usiku wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yoswa atawatumiza, anapita ku malo wokabisalakowo ndipo anadikirira kumeneko. Malowa anali pakati pa Beteli ndi Ai, kumadzulo kwa Ai. Koma Yoswa anagona usiku umenewu pakati pa gulu lake lankhondo. Onani mutuwo |