Yoswa 8:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo kudzali, mutagwira mzinda, muzitentha mzindawo ndi moto; muzichita monga mwa mau a Yehova; taonani, ndakulamulirani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo kudzali, mutagwira mudzi, muzitentha mudziwo ndi moto; muzichita monga mwa mau a Yehova; taonani, ndakulamulirani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mutaulanda, dzauyatseni moto, monga Chauta walamulira. Ameneŵa ndiwo malamulo amene ndakupatsani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mukakawulanda mzindawo mudzawuyatse moto. Mukachite monga mwa mawu a Yehova. Amenewa ndiwo malamulo amene ndakupatsani.” Onani mutuwo |