Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 8:7 - Buku Lopatulika

7 pamenepo muziuka m'molalira ndi kulowa m'mzinda; pakuti Yehova Mulungu wanu; adzaupereka m'manja mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 pamenepo muziuka m'molalira ndi kulowa m'mudzi; pakuti Yehova Mulungu wanu; adzaupereka m'manja mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Pamenepo tsono mudzatuluke kuja mudzakhale mutabisalaku, ndipo mudzalanda mzindawo. Chauta, Mulungu wanu, adzakupatsani mzinda umenewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 inu mudzatuluke pamene mwabisalapo ndi kulanda mzindawo. Yehova Mulungu wanu adzakupatsani mzindawo.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 8:7
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Naamani kazembe wa khamu la nkhondo la mfumu ya Aramu anali munthu womveka pamaso pa mbuyake, ndi waulemu; popeza mwa iye Yehova adapulumutsa Aaramu; ndiyenso ngwazi, koma wakhate.


Pamenepo Yehova anati kwa Yoswa, Usaope, kapena kutenga nkhawa, tenga anthu onse a nkhondo apite nawe, ndipo tauka, kwera ku Ai; taona, ndapereka m'dzanja lako mfumu ya ku Ai, ndi anthu ake ndi mzinda wake ndi dziko lake;


ndipo adzatuluka kutitsata mpaka tidawakokera asiyane ndi mzinda; pakuti adzanena, Atithawa pamaso pathu monga poyamba paja; nafenso tidzathawa pamaso pao;


Ndipo kudzali, mutagwira mzinda, muzitentha mzindawo ndi moto; muzichita monga mwa mau a Yehova; taonani, ndakulamulirani.


Tsono Davide anafunsiranso kwa Yehova. Ndipo Yehova anamyankha iye, nati, Nyamuka, nutsikire ku Keila; pakuti ndidzapereka Afilisti m'dzanja lako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa