Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 8:6 - Buku Lopatulika

6 ndipo adzatuluka kutitsata mpaka tidawakokera asiyane ndi mzinda; pakuti adzanena, Atithawa pamaso pathu monga poyamba paja; nafenso tidzathawa pamaso pao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 ndipo adzatuluka kutitsata mpaka tidawakokera asiyane ndi mudzi; pakuti adzanena, Atithawa pamaso pathu monga poyamba paja; nafenso tidzathawa pamaso pao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Adzatithamangitsa motero, mpaka ife titaona kuti ali kutali ndi mzindawo, chifukwa iwowo azidzati, ‘Akutithaŵa monga kale lija.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Iwo adzatithamangitsa mpaka titawakokera kutali ndi mzindawo, pakuti iwo adzati, ‘Akutithawa monga anachitira poyamba.’ Pamene ife tizidzathawa,

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 8:6
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Farao adzanena za ana a Israele, Azimidwa dziko, chipululu chawatsekera.


Mdani anati, Ndiwalondola, ndiwapeza, ndidzagawa zofunkha; ndidzakhuta nao mtima; ndidzasolola lupanga langa, dzanja langa lidzawaononga.


Popeza sambwezera choipa chake posachedwa atamtsutsa munthu, ana a anthu atsimikizadi mitima yao kuchita zoipa.


Pakuti munthu sadziwatu mphindi yake; monga nsomba zigwidwa mu ukonde woipa, ndi mbalame zikodwa mumsampha, momwemo ana a anthu amagwidwa ndi nthawi ya tsoka, ngati msampha umene uwagwera modzidzimuka.


ndipo ine, ndi anthu onse ali nane, tidzayandikira mzinda; ndipo kudzali, pamene atuluka kudzakomana nafe, monga poyamba paja, tidzathawa pamaso pao;


pamenepo muziuka m'molalira ndi kulowa m'mzinda; pakuti Yehova Mulungu wanu; adzaupereka m'manja mwanu.


Ndipo ana a Benjamini anati, Tawakantha pamaso pathu monga poyamba paja. Koma ana a Israele anati, Tithawe, tiwakokere kutali ndi mzinda kumakwalala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa