Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 8:5 - Buku Lopatulika

5 ndipo ine, ndi anthu onse ali nane, tidzayandikira mzinda; ndipo kudzali, pamene atuluka kudzakomana nafe, monga poyamba paja, tidzathawa pamaso pao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 ndipo ine, ndi anthu onse ali nane, tidzayandikira mudzi; ndipo kudzali, pamene atuluka kudzakomana nafe, monga poyamba paja, tidzathawa pamaso pao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Anthu anga pamodzi ndi ine ndiye tidzayambe kuuputa mzindawo cha kumaso kwake. Tsono akadzangotuluka kuti alimbane nafe, ife tidzabwerera m'mbuyo, monga momwe tidachitira tsiku lina lija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ine ndi gulu langa lonse tikayamba kuwuputa mzindawu, ndipo akadzangotuluka kudzalimbana nafe, ife tidzawathawa monga tinachitira poyamba.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 8:5
4 Mawu Ofanana  

Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu; chifukwa chake khalani ochenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.


Ndipo amuna a ku Ai anawakantha amuna, ngati makumi atatu mphambu asanu ndi mmodzi; nawapirikitsa kuyambira pachipata mpaka ku Sebarimu, nawakantha potsika; ndi mitima ya anthu inasungunuka inga madzi.


ndipo adzatuluka kutitsata mpaka tidawakokera asiyane ndi mzinda; pakuti adzanena, Atithawa pamaso pathu monga poyamba paja; nafenso tidzathawa pamaso pao;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa