Yoswa 8:16 - Buku Lopatulika16 Pamenepo anthu onse okhala m'mzinda, anaitanidwa awapirikitse, nampirikitsa Yoswa, nakokedwa kusiyana ndi mzinda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pamenepo anthu onse okhala m'mudzi, anaitanidwa awapirikitse, nampirikitsa Yoswa, nakokedwa kusiyana ndi mudzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Anthu onse amumzindamo adauzidwa kuti aŵatsate pambuyo, ndipo pamene ankapirikitsa Yoswa, iyeyo ankathaŵira kutsogolo ndithu, kutalikirana ndi mzinda wao uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Anthu onse a ku Ai anawuzidwa kuti awapirikitse. Ndipo iwo anapirikitsadi Yoswa uja, ndi kupita kutali ndi mzinda wawo. Onani mutuwo |