Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 8:11 - Buku Lopatulika

11 Ndi anthu onse a nkhondo okhala naye anakwera, nayandikira nafika pamaso pa mzinda, namanga misasa kumpoto kwa Ai; koma pakati pa iye ndi Ai panali chigwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndi anthu onse a nkhondo okhala naye anakwera, nayandikira nafika pamaso pa mudzi, namanga misasa kumpoto kwa Ai; koma pakati pa iye ndi Ai panali chigwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Ankhondo omwe anali ndi iyeyo adatsogolako, nakamanga zithando chakumpoto kupenyana ndi chipata cha mzindawo. Pakati pa iwowo ndi mzinda wa Aiwo panali chigwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Gulu lonse la nkhondo limene linali ndi iye linatsogolako ndi kukamanga zithando pafupi ndi mzindawo chakumpoto mopenyana nawo. Pakati pa iwo ndi mzindawo panali chigwa.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 8:11
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Yoswa analawira m'mamawa, nayesa anthu, nakwera, iye ndi akulu a Israele, pamaso pa anthu a ku Ai.


Ndipo anatenga amuna ngati zikwi zisanu, nawaika m'molalira pakati pa Betele ndi Ai, kumadzulo kwa mzinda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa