Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 8:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Yoswa analawira m'mamawa, nayesa anthu, nakwera, iye ndi akulu a Israele, pamaso pa anthu a ku Ai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Yoswa analawira m'mamawa, nayesa anthu, nakwera, iye ndi akulu a Israele, pamaso pa anthu a ku Ai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 M'mamaŵa, Yoswa adadzuka naitana ankhondo ake onse. Tsono iyeyo ndi atsogoleri a Aisraele, adapita ku Ai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mmawa mwake, Yoswa anadzuka nayitana asilikali ake. Tsono iye pamodzi ndi akuluakulu a Aisraeli anatsogola kupita ku Ai.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 8:10
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa namanga bulu wake, natengako anyamata ake awiri pamodzi naye, ndi Isaki mwana wake, nawaza nkhuni za nsembe yopsereza, nauka, nanka kumalo komwe Mulungu anamuuza iye.


Ndinafulumira, osachedwa, kusamalira malamulo anu.


Ndipo Yoswa analawirira mamawa, kuchoka ku Sitimu, nafika ku Yordani, iye ndi ana onse a Israele; nagona komweko, asanaoloke.


Ndipo Yoswa analawira mamawa, ndi ansembe anasenza likasa la Yehova.


Ndipo Yoswa analawira mamawa, nayandikizitsa Israele, fuko ndi fuko; ndi fuko la Yuda linagwidwa;


Ndi anthu onse a nkhondo okhala naye anakwera, nayandikira nafika pamaso pa mzinda, namanga misasa kumpoto kwa Ai; koma pakati pa iye ndi Ai panali chigwa.


Ndipo Yoswa anawatuma, namuka iwo kulowa m'molalira, nakhala pakati pa Betele ndi Ai, kumadzulo kwa Ai; koma Yoswa anakhala mwa anthu usiku uja.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa