Yoswa 7:9 - Buku Lopatulika9 Akadzamva ichi Akanani ndi okhala m'dziko onse, adzatizinga ndi kuduliratu dzina lathu padziko lapansi; ndipo mudzachitiranji dzina lanu lalikulu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Akadzamva ichi Akanani ndi okhala m'dziko onse, adzatizinga ndi kuduliratu dzina lathu pa dziko lapansi; ndipo mudzachitiranji dzina lanu lalikulu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Akanani ndi anthu ena onse okhala m'dziko muno adzamva zimenezi, ndipo adzatizinga ndi kutipha tonse. Kodi pamenepa inu mudzachitapo chiyani kuti ulemu wanu usaonongeke?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Akanaani ndi anthu ena a dziko lino adzamva zimenezi ndipo adzatizinga ndi kutiwonongeratu. Nanga inu mudzatani ndi dzina lanu lamphamvulo?” Onani mutuwo |