Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoswa 7:4 - Buku Lopatulika

4 Potero mwa anthu anakwerako amuna monga zikwi zitatu; koma anathawa pamaso pa amuna a ku Ai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Potero mwa anthu anakwerako amuna monga zikwi zitatu; koma anathawa pamaso pa amuna a ku Ai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Motero Yoswa adangotuma anthu ngati zikwi zitatu. Koma tsono anthu a ku Ai adapirikitsa Aisraelewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Choncho kunapita anthu 3,000. Koma iwo anathamangitsidwa ndi anthu a ku Ai.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 7:4
7 Mawu Ofanana  

Munapinditsa kukamwa kwake kwa lupanga lake, osamuimika kunkhondo.


Chikwi chimodzi chidzathawa pakuwadzudzula mmodzi; pakukudzudzulani anthu asanu mudzathawa; kufikira inu mudzasiyidwa ngati mlongoti pamwamba paphiri, ndi ngati mbendera pamwamba pa chitunda.


koma zoipa zanu zakulekanitsani inu ndi Mulungu wanu; ndipo machimo anu abisa nkhope yake kwa inu, kuti Iye sakumva.


Ndipo nkhope yanga idzatsutsana nanu; kuti adani anu adzakukanthani, ndipo akudana ndi inu adzachita ufumu pa inu ndipo mudzathawa wopanda wakukulondolani.


Yehova adzalola adani anu akukantheni; mudzawatulukira njira imodzi, koma mudzawathawa pamaso pao njira zisanu ndi ziwiri, ndipo mudzagwedezeka pakati pa maufumu onse a dziko lapansi.


Mmodzi akadapirikitsa zikwi, awiri akadathawitsa zikwi khumi, akadapanda kuwagulitsa Thanthwe lao, akadapanda kuwapereka Yehova.


Ndipo anabwera kwa Yoswa, nati kwa iye, Asakwere anthu onse; koma akwere amuna ngati zikwi ziwiri kapena zitatu kukantha Ai; musalemetsa anthu onse kunkako, pakuti a komweko ndi owerengeka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa