Yoswa 7:4 - Buku Lopatulika4 Potero mwa anthu anakwerako amuna monga zikwi zitatu; koma anathawa pamaso pa amuna a ku Ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Potero mwa anthu anakwerako amuna monga zikwi zitatu; koma anathawa pamaso pa amuna a ku Ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Motero Yoswa adangotuma anthu ngati zikwi zitatu. Koma tsono anthu a ku Ai adapirikitsa Aisraelewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Choncho kunapita anthu 3,000. Koma iwo anathamangitsidwa ndi anthu a ku Ai. Onani mutuwo |