Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 7:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo Yoswa analawira mamawa, nayandikizitsa Israele, fuko ndi fuko; ndi fuko la Yuda linagwidwa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo Yoswa analawira mamawa, nayandikizitsa Israele, fuko ndi fuko; ndi fuko la Yuda linagwidwa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 M'maŵa mwake Yoswa adadzuka m'mamaŵa, natulutsa Aisraele onse fuko limodzilimodzi. Fuko la Yuda lidalozedwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Mmawa mwake Yoswa anabweretsa Israeli fuko limodzilimodzi ndipo fuko la Yuda linalozedwa.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 7:16
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa namanga bulu wake, natengako anyamata ake awiri pamodzi naye, ndi Isaki mwana wake, nawaza nkhuni za nsembe yopsereza, nauka, nanka kumalo komwe Mulungu anamuuza iye.


Ndinafulumira, osachedwa, kusamalira malamulo anu.


Chilichonse dzanja lako lichipeza kuchichita, uchichite ndi mphamvu yako; pakuti mulibe ntchito ngakhale kulingirira ngakhale kudziwa, ngakhale nzeru, kumanda ulikupitako.


Ndipo Yoswa analawirira mamawa, kuchoka ku Sitimu, nafika ku Yordani, iye ndi ana onse a Israele; nagona komweko, asanaoloke.


Ndipo kudzali kuti iye wogwidwa ali nacho choperekedwacho adzatenthedwa ndi moto, iye ndi zonse ali nazo chifukwa analakwira chipangano cha Yehova, ndi chifukwa anachita chopusa mu Israele.


nayandikizitsa zibale za Yuda, nagwira chibale cha Azera; nayandikizitsa chibale cha Azera, mmodzimmodzi, nagwidwa Zabidi;


Nauka ana a Israele m'mawa, naumangira Gibea misasa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa