Yoswa 7:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Yehova anati kwa Yoswa, Tauka, wagweranji pankhope pako chotere? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Yehova anati kwa Yoswa, Tauka, wagweranji pankhope pako chotere? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chauta adamuuza Yoswa kuti, “Dzuka, chifukwa chiyani wagwada pansi chotere? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Koma Yehova anati kwa Yoswa, “Imirira! Chifukwa chiyani wagwada pansi chotere? Onani mutuwo |