Yoswa 6:7 - Buku Lopatulika7 Nati kwa anthu, Pitani, muzizungulira mzinda, ndi ankhondo ndi zida zao atsogolere likasa la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Nati kwa anthu, Pitani, muzizungulira mudzi, ndi ankhondo ndi zida zao atsogolere likasa la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndipo adauza anthu kuti, “Yambamponi. Yendani mozungulira mzindawo, ankhondo akhale patsogolo pa Bokosi lachipangano.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo analamulira anthu kuti, “Yambani kuyenda! Yendani mozungulira mzinda ndipo ankhondo akhale patsogolo pa Bokosi la Yehova.” Onani mutuwo |