Yoswa 6:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Yehova ananena kwa Yoswa, Taona, ndapereka m'dzanja lako Yeriko ndi mfumu yake, ndi ngwazi zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Yehova ananena kwa Yoswa, Taona, ndapereka m'dzanja lako Yeriko ndi mfumu yake, ndi ngwazi zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta adauza Yoswa kuti, “Mvetsa! Yeriko, pamodzi ndi mfumu yake ndi ankhondo ake amphamvu, ndakupatsa iwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kenaka Yehova anati kwa Yoswa, “Taona ndapereka Yeriko, pamodzi ndi mfumu yake ndi ankhondo ake mʼmanja mwako. Onani mutuwo |