Yoswa 6:1 - Buku Lopatulika1 Koma ku Yeriko anatseka pazipata, natsekedwa chifukwa cha ana a Israele, panalibe wotuluka, panalibenso wolowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma ku Yeriko anatseka pazipata, natsekedwa chifukwa cha ana a Israele, panalibe wotuluka, panalibenso wolowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mzinda wa Yeriko udaali utatsekedwa pa zipata zake zonse, kuti Aisraele asaloŵe. Panalibe ndi mmodzi yemwe wotuluka kapena kuloŵa mumzindamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsono mzinda wa Yeriko unali utatsekedwa kuti Aisraeli asalowe. Palibe amene amatuluka kapena kulowa. Onani mutuwo |