Yoswa 5:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yehova anati kwa Yoswa, Lero lino ndakukunkhunizirani mtonzo wa Ejipito. Chifukwa chake dzina la malowo analitcha Giligala kufikira lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yehova anati kwa Yoswa, Lero lino ndakukunkhunizirani mtonzo wa Ejipito. Chifukwa chake dzina la malowo analitcha Giligala kufikira lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono Chauta adauza Yoswa kuti, “Lero ndakuchotserani manyazi a ukapolo wanu uja umene munali nawo ku Ejipito.” Nchifukwa chake malowo adaŵatcha Giligala, ndipo mpaka lero lino malo ameneŵa akudziŵika ndi dzina limeneli. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kenaka Yehova anati kwa Yoswa, “Kuyambira tsopano anthu a ku Igupto sadzakunyozaninso.” Nʼchifukwa chake malowa anatchedwa Giligala mpaka lero. Onani mutuwo |