Yoswa 5:4 - Buku Lopatulika4 Koma chifukwa chakuti Yoswa anawadula ndi ichi: anthu onse otuluka mu Ejipito, anthu aamuna, ndiwo amuna onse ankhondo, adafa m'chipululu panjira, atatuluka mu Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma chifukwa chakuti Yoswa anawadula ndi ichi: anthu onse otuluka m'Ejipito, anthu amuna, ndiwo amuna onse ankhondo, adafa m'chipululu panjira, atatuluka m'Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adachita zimenezi chifukwa amuna amene anali oyenera kuponya nkhondo onse adaatha nkufa m'chipululu atatuluka ku Ejipito kuja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Chifukwa chimene Yoswa anachitira izi ndi ichi: Onse amene anatuluka mʼdziko la Igupto, amuna onse amene anali oyenera kumenya nkhondo anatha kufa mʼchipululu atatuluka mʼdziko la Igupto. Onani mutuwo |