Yoswa 5:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Yoswa anadzisemera mipeni yamiyala nadula ana a Israele pa Gibea-Naraloti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Yoswa anadzisemera mipeni yamiyala nadula ana a Israele pa Gibea-Naraloti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Yoswa adasemadi mipeni yamiyalayo, naŵaumbala onsewo ku phiri lotchedwa “Koumbalira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Choncho Yoswa anapanga mipeni ya miyala ndi kuchita mdulidwe Aisraeli ku Gibeyati Haaraloti. Onani mutuwo |