Yoswa 5:2 - Buku Lopatulika2 Nthawi imeneyo Yehova anati kwa Yoswa, Udzisemere mipeni yamiyala nudulenso ana a Israele kachiwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nthawi imeneyo Yehova anati kwa Yoswa, Udzisemere mipeni yamiyala nudulenso ana a Israele kachiwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Chauta adauza Yoswa kuti, “Sema miyala ngati mipeni, kuti uumbalire Aisraeleŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tsono Yehova anati kwa Yoswa, “Panga mipeni ya miyala ndipo uchitenso mwambo wa mdulidwe pa Aisraeli.” Onani mutuwo |