Yoswa 5:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo kunali, pamene mafumu onse a Aamori okhala tsidya la kumadzulo la Yordani, ndi mafumu onse a Akanani okhala ku nyanja anamva kuti Yehova anaphwetsa madzi a Yordani pamaso pa ana a Israele mpaka titaoloka, mtima wao unasungunuka, analibenso moyo chifukwa cha ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo kunali, pamene mafumu onse a Aamori okhala tsidya la kumadzulo la Yordani, ndi mafumu onse a Akanani okhala ku nyanja anamva kuti Yehova anaphwetsa madzi a Yordani pamaso pa ana a Israele mpaka titaoloka, mtima wao unasungunuka, analibenso moyo chifukwa cha ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mafumu onse a Aamori amene ankakhala kuzambwe kwa Yordani, pamodzi ndi mafumu a Akanani okhala m'mphepete mwa nyanja, adamva kuti Chauta adaumitsa Yordani pamene Aisraele ankaoloka. Choncho adachita mantha, ndi kutayiratu mtima chifukwa cha Aisraelewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mafumu onse a Aamori, a kummawa kwa Yorodani ndi mafumu onse a Akanaani a mʼmbali mwa Nyanja anamva momwe Yehova anawumitsira Yorodani pamene Aisraeli ankawoloka. Choncho anachita mantha ndi kutayiratu mtima chifukwa cha Aisraeliwo. Onani mutuwo |