Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 4:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo ana a Israele anachita monga Yoswa anawalamulira, nasenza miyala khumi ndi iwiri pakati pa Yordani, monga Yehova adalankhula ndi Yoswa, monga mwa kuwerenga kwa mafuko a ana a Israele; ndipo anaoloka nayo kunka kogona, naiika komweko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo ana a Israele anachita monga Yoswa anawalamulira, nasenza miyala khumi ndi iwiri pakati pa Yordani, monga Yehova adalankhula ndi Yoswa, monga mwa kuwerenga kwa mafuko a ana a Israele; ndipo anaoloka nayo kunka kogona, naiika komweko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Anthuwo adachitadi zonse zimene Yoswa adaŵalamula. Adanyamula miyala khumi ndi iŵiri pakati pa mtsinje wa Yordani, monga momwe Chauta adalamulira Yoswa. Anthu a fuko lililonse la Aisraele adanyamula mwala umodzi. Miyalayo adapita nayo kukaikhazika pansi pamalo pamene panali zithando paja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Aisraeli anachitadi monga Yoswa anawalamulira. Iwo ananyamula miyala khumi ndi iwiri kuchokera pakati pa Yorodani, fuko lililonse la Israeli mwala wake, monga Yehova analamulira Yoswa. Miyalayo anapita nayo ku misasa yawo nakayikhazika kumeneko.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 4:8
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu anawerama, nalambira. Ndipo ana a Israele anamuka nachita monga Yehova adalamulira Mose ndi Aroni; anachita momwemo.


Ndipo Mose analembera mau onse a Yehova, nalawira kuuka mamawa, namanga guwa la nsembe patsinde paphiri, ndi zoimiritsa khumi ndi ziwiri, kwa mafuko khumi ndi awiri a Israele.


Ndipo Yoswa anaimika ku Giligala miyala ija khumi ndi iwiri adaitenga mu Yordani.


Ndipo Yoswa anaimika miyala khumi ndi iwiri pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe akusenza likasa la chipangano; ikhala komweko kufikira lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa