Yoswa 4:7 - Buku Lopatulika7 Munene nao, Chifukwa madzi a Yordani anadulidwa patsogolo pa likasa la chipangano cha Yehova; muja lidaoloka Yordani, madzi a Yordani anadulidwa; ndipo miyala iyi idzakhala chikumbutso cha ana a Israele chikhalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Munene nao, Chifukwa madzi a Yordani anadulidwa patsogolo pa likasa la chipangano cha Yehova; muja lidaoloka Yordani, madzi a Yordani anadulidwa; ndipo miyala iyi idzakhala chikumbutso cha ana a Israele chikhalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 muzidzaŵauza kuti, ‘Madzi a Yordani adaaima osayendanso, pamene Bokosi lachipangano la Chauta linkaoloka mtsinjewu.’ Miyala imeneyi idzakhala chikumbutso kwa Aisraele.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Muzidzawawuza kuti, ‘Madzi a Yorodani analeka kuyenda pamene Bokosi la Chipangano la Yehova linkawoloka mtsinjewo. Miyala iyi idzakhala chikumbutso kwa anthu a Israeli kwa muyaya.’ ” Onani mutuwo |