Yoswa 4:6 - Buku Lopatulika6 kuti ichi chikhale chizindikiro pakati pa inu. Akakufunsani ana anu m'tsogolomo, ndi kuti, Miyala iyi nja chiyani ndi inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 kuti ichi chikhale chizindikiro pakati pa inu. Akakufunsani ana anu m'tsogolomo, ndi kuti, Miyala iyi nja chiyani ndi inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Miyala imeneyi idzakhala chikumbutso, ndipo anthu azidzakumbukira zimene Chauta wachita. Ana anu akamadzakufunsani m'tsogolo muno tanthauzo lake la miyala imeneyi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 kuti ikhale chizindikiro kwa inu. Mʼtsogolo muno ana anu akamadzakufunsani kuti, ‘Kodi miyala iyi ikutanthauza chiyani?’ Onani mutuwo |