Yoswa 4:5 - Buku Lopatulika5 nanena nao Yoswa, Olokani, kutsogolera likasa la Yehova Mulungu wanu pakati pa Yordani, nimudzisenzere yense mwala paphewa pake, monga mwa kuwerenga kwa mafuko a ana a Israele; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 nanena nao Yoswa, Olokani, kutsogolera likasa la Yehova Mulungu wanu pakati pa Yordani, nimudzisenzere yense mwala paphewa pake, monga mwa kuwerenga kwa mafuko a ana a Israele; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 ndipo adaŵalamula kuti, “Loŵani mu mtsinje wa Yordaniwu patsogolo pa Bokosi lachipangano la Chauta, Mulungu wanu. Aliyense mwa inu atenge mwala pa phewa. Fuko lililonse la Aisraele litenge mwala umodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 ndipo anawawuza kuti, “Lowani pakati pa mtsinje wa Yorodani, patsogolo pa Bokosi la Yehova Mulungu wanu. Ndipo aliyense wa inu atenge mwala pa phewa lake, monga mwa chiwerengero cha mafuko a Aisraeli, Onani mutuwo |