Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoswa 4:4 - Buku Lopatulika

4 Pamenepo Yoswa anaitana amuna khumi ndi awiriwo amene anawaikiratu mwa ana a Israele, fuko limodzi mwamuna mmodzi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Pamenepo Yoswa anaitana amuna khumi ndi awiriwo amene anawaikiratu mwa ana a Israele, fuko limodzi mwamuna mmodzi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Yoswa adaitana amuna khumi ndi aŵiri adaŵasankha aja,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Choncho Yoswa anayitana amuna khumi ndi awiri amene anawasankha aja kuchokera pakati pa Aisraeli, mmodzi pa fuko lililonse,

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 4:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo tsono, mudzitengere amuna khumi ndi awiri mwa mafuko a Israele, fuko limodzi mwamuna mmodzi.


Mudzitengere mwa anthu, amuna khumi ndi awiri, fuko limodzi mwamuna mmodzi;


ndipo muwalamulire iwo ndi kuti, Mudzitengere pano pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe, miyala khumi ndi iwiri, ndi kuoloka nayo, ndi kuiika m'mogona m'mene mugonamo usiku uno.


nanena nao Yoswa, Olokani, kutsogolera likasa la Yehova Mulungu wanu pakati pa Yordani, nimudzisenzere yense mwala paphewa pake, monga mwa kuwerenga kwa mafuko a ana a Israele;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa