Yoswa 4:4 - Buku Lopatulika4 Pamenepo Yoswa anaitana amuna khumi ndi awiriwo amene anawaikiratu mwa ana a Israele, fuko limodzi mwamuna mmodzi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pamenepo Yoswa anaitana amuna khumi ndi awiriwo amene anawaikiratu mwa ana a Israele, fuko limodzi mwamuna mmodzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Yoswa adaitana amuna khumi ndi aŵiri adaŵasankha aja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Choncho Yoswa anayitana amuna khumi ndi awiri amene anawasankha aja kuchokera pakati pa Aisraeli, mmodzi pa fuko lililonse, Onani mutuwo |