Yoswa 4:3 - Buku Lopatulika3 ndipo muwalamulire iwo ndi kuti, Mudzitengere pano pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe, miyala khumi ndi iwiri, ndi kuoloka nayo, ndi kuiika m'mogona m'mene mugonamo usiku uno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndipo muwalamulire iwo ndi kuti, Mudzitengere pano pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe, miyala khumi ndi iwiri, ndi kuoloka nayo, ndi kuiika m'mogona m'mene mugonamo usiku uno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono uŵalamule kuti, ‘Tengani miyala khumi ndi iŵiri pakati penipeni pa mtsinje wa Yordanipo, pa malo amene anali kuimirira ansembewo. Nyamulani miyala imeneyo ndi kudza nayo ku zithando zanu kumene mudzagone usiku.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono uwalamule kuti, ‘Tengani miyala khumi ndi iwiri pakati penipeni pa mtsinje wa Yorodani, pamalo pamene ansembe anayimirirapo. Miyalayo muwoloke nayo ndi kudzayitula pamalo pamene mukagone usiku uno.’ ” Onani mutuwo |