Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoswa 4:2 - Buku Lopatulika

2 Mudzitengere mwa anthu, amuna khumi ndi awiri, fuko limodzi mwamuna mmodzi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Mudzitengere mwa anthu, amuna khumi ndi awiri, fuko limodzi mwamuna mmodzi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Sankha amuna khumi ndi aŵiri, mmodzi pa fuko lililonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Sankha amuna khumi ndi awiri, mmodzi pa fuko lililonse.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 4:2
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Eliya anatenga miyala khumi ndi iwiri, monga mwa ziwerengo cha mafuko ana a Yakobo, amene mau a Yehova adamfikira, kuti, Dzina lako ndi Israele.


Udzitumire amuna, kuti azonde dziko la Kanani, limene ndilikupatsa ana a Israele; utumize munthu mmodzi wa fuko lililonse la makolo ao, yense kalonga pakati pa anzake.


Muwatengenso akalonga, kalonga mmodzi ku fuko limodzi, agawe dziko likhale cholowa chao.


Ndipo chinandikomera chinthu ichi; ndipo ndinatenga amuna khumi ndi awiri a inu, fuko limodzi mwamuna mmodzi;


Ndipo tsono, mudzitengere amuna khumi ndi awiri mwa mafuko a Israele, fuko limodzi mwamuna mmodzi.


ndipo muwalamulire iwo ndi kuti, Mudzitengere pano pakati pa Yordani, poimapo mapazi a ansembe, miyala khumi ndi iwiri, ndi kuoloka nayo, ndi kuiika m'mogona m'mene mugonamo usiku uno.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa